1 Akorinto 12:11 - Buku Lopatulika11 Koma zonse izi achita Mzimu mmodzi yemweyo, nagawira yense pa yekha monga afuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma zonse izi achita Mzimu mmodzi yemweyo, nagawira yense pa yekha monga afuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Amene amachititsa anthu zonsezi ndi Mzimu Woyera mmodzi yemweyo. Amagaŵira munthu aliyense monga momwe Iye afuna kumgaŵira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Zonsezi ndi ntchito za Mzimu mmodzi yemweyo, ndipo amapereka kwa munthu aliyense monga momwe Mzimuyo wafunira. Onani mutuwo |