1 Akorinto 11:5 - Buku Lopatulika5 Koma mkazi yense wakupemphera, kapena kunenera, wovula mutu, anyoza mutu wake; pakuti kuli chimodzimodzi kumetedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma mkazi yense wakupemphera, kapena kunenera, wovula mutu, anyoza mutu wake; pakuti kuli chimodzimodzi kumetedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma mkazi akamapemphera kapena kulalika mau a Mulungu, osavala kanthu kumutu, akunyoza mutu wake. Kuteroko sikusiyana ndi kungometa mpala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo mkazi aliyense wopemphera kapena kunenera asanaphimbe mutu wake sakulemekeza mutu wakewo. Kuli chimodzimodzi kumeta mutu wake. Onani mutuwo |