1 Akorinto 11:4 - Buku Lopatulika4 Mwamuna yense woveka mutu, popemphera kapena ponenera, anyoza mutu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mwamuna yense woveka mutu, popemphera kapena ponenera, anyoza mutu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ngati mwamuna apemphera kapena kulalika mau a Mulungu, atavala kanthu kumutu, akunyoza mutu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mwamuna aliyense wopemphera kapena kunenera ataphimba mutu wake akunyoza mutu wakewo. Onani mutuwo |