Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 11:1 - Buku Lopatulika

1 Khalani onditsanza ine, monga inenso nditsanza Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Khalani onditsanza ine, monga inenso nditsanza Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Muzinditsanzira ine monga momwe inenso ndimatsanzira Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Tsatirani chitsanzo changa, monga inenso nditsatira chitsanzo cha Khristu.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 11:1
9 Mawu Ofanana  

monga inenso ndikondweretsa onse m'zinthu zonse, wosafuna chipindulo changa, koma cha unyunjiwo, kuti apulumutsidwe.


Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.


Abale, khalani pamodzi akutsanza anga, ndipo yang'anirani iwo akuyenda kotero monga muli ndi ife chitsanzo chanu.


Ndipo munayamba kukhala akutsanza athu, ndi a Ambuye, m'mene mudalandira mauwo m'chisautso chambiri, ndi chimwemwe cha Mzimu Woyera;


si chifukwa tilibe ulamuliro, komatu kuti tidzipereke tokha tikhale kwa inu chitsanzo chanu, kuti mukatitsanze ife.


kuti musakhale aulesi, koma akuwatsanza iwo amene alikulowa malonjezano mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa