1 Akorinto 10:32 - Buku Lopatulika32 Khalani osakhumudwitsa, kapena Ayuda, kapena Agriki, kapena Mpingo wa Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Khalani osakhumudwitsa, kapena Ayuda, kapena Agriki, kapena Mpingo wa Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Moyo wanu ukhale wosaphunthwitsa Ayuda, kapena anthu a mitundu ina, kapenanso Mpingo wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Musakhumudwitse aliyense, kaya ndi Myuda, Mgriki, kapena mpingo wa Mulungu. Onani mutuwo |