1 Akorinto 10:23 - Buku Lopatulika23 Zinthu zonse ziloleka; koma sizipindula zonse. Zinthu zonse ziloleka; koma sizimanga zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Zinthu zonse ziloleka; koma sizipindula zonse. Zinthu zonse ziloleka; koma sizimanga zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Zinthu zonse nzololedwa, koma si zonse zili ndi phindu. Zonse nzololedwa, koma si zonse zimathandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Mutha kunena kuti, “Zinthu zonse nʼzololedwa,” komatu si zonse zili za phindu. “Zinthu zonse nʼzololedwa,” komatu si zonse zimathandiza. Onani mutuwo |