1 Akorinto 10:14 - Buku Lopatulika14 Chifukwa chake, okondedwa anga, thawani kupembedza mafano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chifukwa chake, okondedwa anga, thawani kupembedza mafano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono okondedwa anga, pewani kupembedza mafano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Choncho abwenzi anga okondedwa, lekani kupembedza mafano. Onani mutuwo |