1 Akorinto 10:1 - Buku Lopatulika1 Pakuti sindifuna, kuti mukhale osadziwa, abale, kuti makolo athu onse anali pansi pa mtambo, naoloka nyanja onse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pakuti sindifuna, kuti mukhale osadziwa, abale, kuti makolo athu onse anali pansi pa mtambo, naoloka nyanja onse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Abale, ndifuna kuti mudziŵe zimene zidaŵachitikira makolo athu akale aja. Onse adayenda mu mthunzi wa mtambo, ndipo onse adaoloka Nyanja Yofiira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pakuti sindikufuna kuti inu mukhale osadziwa zenizeni, abale, kuti makolo athu anatsogozedwa ndi mtambo ndikuti onse anawoloka nyanja. Onani mutuwo |