1 Akorinto 1:23 - Buku Lopatulika23 koma ife tilalikira Khristu wopachikidwa, kwa Ayudatu chokhumudwitsa, ndi kwa amitundu chinthu chopusa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 koma ife tilalikira Khristu wopachikidwa, kwa Ayudatu chokhumudwitsa, ndi kwa amitundu chinthu chopusa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Koma ife timalalika Khristu amene adapachikidwa pa mtanda. Kwa Ayuda mau ameneŵa ndi okhumudwitsa, pamene kwa anthu a mitundu ina mauŵa ndi opusa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 koma ife timalalikira Khristu wopachikidwa. Chitsa chokhumudwitsa kwa Ayuda ndi chopusa kwa a mitundu ina. Onani mutuwo |