1 Akorinto 1:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ayuda amafuna kuwona zozizwitsa, pamene Agriki amafunafuna nzeru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ayuda amafuna zizindikiro zodabwitsa ndipo Agriki amafunafuna nzeru, Onani mutuwo |