Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 1:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ayuda amafuna kuwona zozizwitsa, pamene Agriki amafunafuna nzeru.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ayuda amafuna zizindikiro zodabwitsa ndipo Agriki amafunafuna nzeru,

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 1:22
10 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anapatsa chizindikiro tsiku lomwelo, nati, Chizindikiro chimene Yehova ananena ndi ichi, Taonani guwali la nsembe lidzang'ambika, ndi phulusa lili pa ilo lidzatayika.


Ndipo Afarisi anatuluka, nayamba kufunsana naye, ndi kufuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba, namuyesa Iye.


Koma ena anamuyesa, nafuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba.


Koma ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi chala cha Mulungu, pamenepo Ufumu wa Mulungu wafikira inu.


Chifukwa chake Ayuda anayankha nati kwa Iye, Mutionetsera ife chizindikiro chanji, pakuti muchita izi?


Pamenepo mkazi anasiya mtsuko wake, namuka mumzinda, nanena ndi anthu,


Pamenepo Yesu anati kwa iye, Ngati simuona zizindikiro ndi zozizwa, simudzakhulupirira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa