Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yuda 1:22 - Buku Lopatulika

Ndipo ena osinkhasinkha muwachitire chifundo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ena osinkhasinkha muwachitire chifundo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pali ena amene ali okayika, amenewo muziŵachitira chifundo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Muwachitire chifundo amene akukayika.

Onani mutuwo



Yuda 1:22
10 Mawu Ofanana  

Ndipo inu, gulu langa, atero Ambuye Yehova, ndiweruza pakati pa zoweta ndi zoweta, nkhosa zamphongo ndi atonde.


Chifukwa chake ndikupemphani inu kuti mumtsimikizire ameneyo chikondi chanu.


koma mwenzi nditakhala nanu tsopano, ndi kusintha mau anga; chifukwa ndisinkhasinkha nanu.


Abale, ngatinso munthu agwidwa nako kulakwa kwakuti, inu auzimu, mubweze wotereyo mu mzimu wa chifatso; ndi kudzipenyerera wekha, ungayesedwe nawenso.


mudzisunge nokha m'chikondi cha Mulungu, ndi kulindira chifundo cha Ambuye wathu Yesu Khristu, kufikira moyo wosatha.


koma ena muwapulumutse ndi kuwakwatula kumoto; koma ena muwachitire chifundo ndi mantha, nimudane naonso malaya ochitidwa mawanga ndi thupi.