Yuda 1:21 - Buku Lopatulika21 mudzisunge nokha m'chikondi cha Mulungu, ndi kulindira chifundo cha Ambuye wathu Yesu Khristu, kufikira moyo wosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 mudzisunge nokha m'chikondi cha Mulungu, ndi kulindira chifundo cha Ambuye wathu Yesu Khristu, kufikira moyo wosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mudzisunge m'chikondi cha Mulungu podikira moyo wosatha, umene Ambuye athu Yesu Khristu adzakupatseni mwa chifundo chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. Onani mutuwo |