Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:9 - Buku Lopatulika

Ndipo m'mene adanena nao zimenezi anakhalabe mu Galileya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'mene adanena nao zimenezi anakhalabe m'Galileya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu atanena zimenezo, adatsalira m'Galileya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atanena izi, Iye anakhalabe mu Galileya.

Onani mutuwo



Yohane 7:9
2 Mawu Ofanana  

Koma pamene abale ake adakwera kunka kuchikondwerero, pomwepo Iyenso anakwera, si poonekera, koma monga mobisalika.


Kwerani inu kunka kuphwando; sindikwera Ine kuphwando ili tsopano apa; pakuti nthawi yanga siinakwanire.