Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 15:3 - Buku Lopatulika

Mwakhala okonzeka tsopano inu chifukwa cha mau amene ndalankhula ndi inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mwakhala okonzeka tsopano inu chifukwa cha mau amene ndalankhula ndi inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu mwayera kale chifukwa cha mau amene ndakuuzani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu ndinu oyera kale chifukwa cha mawu amene ndayankhula inu.

Onani mutuwo



Yohane 15:3
6 Mawu Ofanana  

Yesu ananena naye, Amene anatha kusamba alibe kusowa koma kusamba mapazi, koma ayera monse: ndipo inu ndinu oyera, koma si nonse ai.


Nthambi iliyonse ya mwa Ine yosabala chipatso, aichotsa; ndi iliyonse yakubala chipatso, aisadza, kuti ikabale chipatso chochuluka.


Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi.


Ndipo chifukwa cha iwo Ine ndidzipatula ndekha kuti iwonso akhale opatulidwa m'choonadi.


kuti akampatule, atamyeretsa ndi kumsambitsa madzi ndi mau;


Popeza mwayeretsa moyo wanu pakumvera choonadi kuti mukakonde abale ndi chikondi chosanyenga, mukondane kwenikweni kuchokera kumtima;