Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 9:4 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele, kuti achite Paska.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele, kuti achite Paska.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Mose adauza Aisraele kuti azichita Paska.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Mose anawuza Aisraeli kuti azichita Paska,

Onani mutuwo



Numeri 9:4
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo Mose anaitana akulu onse a Israele, nanena nao, Pitani, dzitengereni anaankhosa monga mwa mabanja anu, nimuphere Paska.


Tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, muziuchita, pa nyengo yake yoikidwa; muuchite monga mwa malemba ake onse, ndi maweruzo ake onse.


Ndipo anachita Paska mwezi woyamba, tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo m'chipululu cha Sinai; monga mwa zonse Yehova adauza Mose, momwemo ana a Israele anachita.