Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:80 - Buku Lopatulika

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaperekanso kambale kamodzi kagolide ka magaramu 110, kodzadza ndi lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;

Onani mutuwo



Numeri 7:80
2 Mawu Ofanana  

chopereka chake ndicho mbale imodzi yasiliva, kulemera kwake masekeli zana limodzi ndi makumi atatu, mbale yowazira imodzi yasiliva ya masekeli makumi asanu ndi awiri, kuyesa sekeli wa malo opatulika; zonse ziwiri zodzala ndi ufa wosakaniza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa;


ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwanawankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, zikhale nsembe yopsereza;