Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:64 - Buku Lopatulika

tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaperekanso tonde mmodzi woperekera nsembe yopepesera machimo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;

Onani mutuwo



Numeri 7:64
2 Mawu Ofanana  

ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwanawankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, zikhale nsembe yopsereza;


Ameneyo sanadziwe uchimo anamyesera uchimo m'malo mwathu; kuti ife tikhale chilungamo cha Mulungu mwa Iye.