Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:20 - Buku Lopatulika

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaperekanso kambale kamodzi kagolide ka magaramu 110, kodzadza ndi lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110 yodzaza ndi lubani;

Onani mutuwo



Numeri 7:20
3 Mawu Ofanana  

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;


anabwera nacho chopereka chake mbale imodzi yasiliva, kulemera kwake masekeli zana limodzi ndi makumi atatu, mbale yowazira imodzi yasiliva ya masekeli makumi asanu ndi awiri, kuyesa sekeli wa malo opatulika; zonse ziwiri zodzala ndi ufa wosakaniza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa;


ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwanawankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, zikhale nsembe yopsereza;