Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 5:12 - Buku Lopatulika

Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wamwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wa mwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Uza Aisraele kuti, mwina mkazi adzazembera mwamuna wake namachita zosakhulupirika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati mkazi wa munthu wina ayenda njira yosayenera nakhala wosakhulupirika kwa mwamuna wake,

Onani mutuwo



Numeri 5:12
6 Mawu Ofanana  

Usachite chigololo.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Ichi ndi chilamulo cha nsanje, pamene mkazi, pokhala naye mwamuna wake, ampatukira nadetsedwa;


Munthu akatenga mkazi akhale wake, kudzali, ngati sapeza ufulu pamaso pake, popeza anapeza mwa iye kanthu kosayenera, amlembere kalata ya chilekanitso, ndi kumpereka uyu m'dzanja lake, ndi kumtulutsa m'nyumba mwake.