Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:12 - Buku Lopatulika

Nachokera ku chipululu cha Sini, nayenda namanga mu Dofika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku chipululu cha Sini, nayenda namanga m'Dofika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku chipululu cha Sini, nakamanga mahema ao ku Dofika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku chipululu cha Sini anakamanga ku Dofika.

Onani mutuwo



Numeri 33:12
3 Mawu Ofanana  

Ndipo khamu lonse la ana a Israele linachoka m'chipululu cha Sini, M'zigono zao, monga mwa mau a Yehova, nagona mu Refidimu. Koma kumeneko kunalibe madzi akumwa anthu.


Nachokera ku Nyanja Yofiira, nayenda namanga m'chipululu cha Sini.


Nachokera ku Dofika, nayenda namanga mu Alusi.