Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:18 - Buku Lopatulika

Sitidzabwerera kwathu, kufikira ana a Israele atalandira yense cholowa chake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Sitidzabwerera kwathu, kufikira ana a Israele atalandira yense cholowa chake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Sitidzabwerera kwathu mpaka Mwisraele aliyense atalandira choloŵa chake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sitidzabwerera ku midzi yathu mpaka Mwisraeli aliyense atalandira cholowa chake.

Onani mutuwo



Numeri 32:18
2 Mawu Ofanana  

kufikira Yehova atapumulitsa abale anu, monga anapumulitsa inu, nalandira iwonso dziko limene Yehova Mulungu wanu awapatsa tsidya lija la Yordani; pamenepo mudzabwerera munthu yense ku cholowa chake, chimene ndinakupatsani.