Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:24 - Buku Lopatulika

Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Eliyasafu mwana wa Laele ndiye anali mtsogoleri wa banja la makolo a Ageresoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mtsogoleri wa mabanja a Ageresoni anali Eliyasafu mwana wa Laeli.

Onani mutuwo



Numeri 3:24
3 Mawu Ofanana  

Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa chihema kumadzulo.


Ndipo udikiro wa ana a Geresoni m'chihema, chokomanako ndiwo Kachisi, ndi chihema, chophimba chake, ndi nsalu yotsekera pa khomo la chihema chokomanako,


Werenganso ana a Geresoni, monga mwa nyumba za makolo ao, monga mwa mabanja ao.