Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 29:4 - Buku Lopatulika

ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndiponso wa kilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiri aja muzipereka kilogalamu imodzi.

Onani mutuwo



Numeri 29:4
2 Mawu Ofanana  

ndi nsembe yao yaufa, ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, atatu a magawo khumi akhale a ng'ombeyo, awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo,


ndi tonde mmodzi wa nsembe yauchimo, yakutetezera inu;