Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 27:8 - Buku Lopatulika

Ndipo unene ndi ana a Israele, ndi kuti, Akafa munthu wamwamuna wopanda mwana wamwamuna, cholowa chake achilandire mwana wake wamkazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo unene ndi ana a Israele, ndi kuti, Akafa munthu wamwamuna wopanda mwana wamwamuna, cholowa chake achilandire mwana wake wamkazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo uŵauze Aisraele kuti, ‘Munthu akafa opanda mwana wamwamuna, choloŵa chake chikhale cha mwana wake wamkazi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Uza Aisraeli kuti, ‘Ngati munthu afa wosasiya mwana wamwamuna, muzipereka cholowa chake kwa mwana wake wamkazi.

Onani mutuwo



Numeri 27:8
2 Mawu Ofanana  

Ana aakazi a Zelofehadi anena zoona; uwapatse ndithu cholowa chikhale chaochao pakati pa abale a atate wao; nuwalandiritse cholowa cha atate wao.


Ndipo akapanda kukhala naye mwana wamkazi, mupatse abale ake cholowa chake.