Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:47 - Buku Lopatulika

Iwo ndiwo mabanja a ana aamuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iwo ndiwo mabanja a ana amuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ameneŵa, anthu okwanira 53,400, ndiwo adaŵerengedwa pa mabanja a Asere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Awa ndiwo anali mafuko a Aseri. Onse amene anawerengedwa analipo 53,400.

Onani mutuwo



Numeri 26:47
3 Mawu Ofanana  

Ndipo dzina la mwana wamkazi wa Asere ndiye Sera.