Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:43 - Buku Lopatulika

Mabanja onse a Asuhamu monga mwa owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mabanja onse a Asuhamu monga mwa owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu oŵerengedwa pa mabanja onse a Suhamu adakwanira 64,400.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Onse a fuko la Asuhamu amene anawerengedwa analipo 64,400.

Onani mutuwo



Numeri 26:43
3 Mawu Ofanana  

Mwana wamwamuna wa Dani monga mwa mabanja ake ndiye Suhamu, ndiye kholo la banja la Asuhamu. Iwo ndiwo mabanja a Dani monga mwa mabanja ao.