Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:27 - Buku Lopatulika

Iwo ndiwo mabanja a Zebuloni monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iwo ndiwo mabanja a Zebuloni monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ameneŵa, anthu okwanira 60,500, ndiwo anali a m'mabanja a Zebuloni, amene adaŵerengedwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Awa ndiwo anali mafuko a Zebuloni. Amene anawerengedwa analipo 60,500.

Onani mutuwo



Numeri 26:27
2 Mawu Ofanana