Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:25 - Buku Lopatulika

Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ameneŵa, anthu okwanira 64,300, ndiwo anali a m'mabanja a Isakara, amene adaŵerengedwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Awa ndi amene anali a fuko la Isakara. Amene anawerengedwa analipo 64,300.

Onani mutuwo



Numeri 26:25
3 Mawu Ofanana  

Yasubu, ndiye kholo la banja la Ayasubu; Simironi, ndiye kholo la banja la Asimironi.