Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 22:21 - Buku Lopatulika

Pamenepo Balamu anauka m'mawa namanga bulu wake, namuka nao akalonga a ku Mowabu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Balamu anauka m'mawa namanga bulu wake, namuka nao akalonga a ku Mowabu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Balamu, atadzuka m'maŵa mwake, adaika chishalo pa bulu wake, ndipo adanyamuka pamodzi ndi akalonga aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Balaamu anadzuka mmawa, namanga bulu wake wamkazi ndipo anapita ndi akuluakulu a Mowabu.

Onani mutuwo



Numeri 22:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa namanga bulu wake, natengako anyamata ake awiri pamodzi naye, ndi Isaki mwana wake, nawaza nkhuni za nsembe yopsereza, nauka, nanka kumalo komwe Mulungu anamuuza iye.


Woyenda mwangwiro adzapulumuka; koma wokhota m'mayendedwe ake adzagwa posachedwa.


posiya njira yolunjika, anasokera, atatsata njira ya Balamu mwana wa Beori, amene anakonda mphotho ya chosalungama;


koma anadzudzulidwa pa kulakwa kwake mwini; bulu wopanda mau, wolankhula ndi mau a munthu, analetsa kuyaluka kwa mneneriyo.