Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 22:15 - Buku Lopatulika

Koma Balaki anaonjeza kutumanso akalonga, ochuluka, ndi omveka koposa awa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Balaki anaonjeza kutumanso akalonga, ochuluka, ndi omveka koposa awa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Balaki adatumanso akalonga ochuluka ndi olemekezeka kopambana oyamba aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Balaki anatumanso akuluakulu ena ambiri ndi olemekezeka kwambiri kuposa oyamba aja ndipo

Onani mutuwo



Numeri 22:15
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo akalonga a Mowabu ananyamuka, nafika kwa Balaki, nati Alikukana Balamu kudza nafe.


Ndipo anadza kwa Balamu, nati kwa iye, Atero Balaki mwana wa Zipori, Pasakhaletu chinthu chakukuletsa kudza kwa ine;