Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:19 - Buku Lopatulika

atachoka ku Matana ku Nahaliyele; atachoka ku Nahaliyele ku Bamoti;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

atachoka ku Matana ku Nahaliyele; atachoka ku Nahaliyele ku Bamoti;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kuchokera ku Matana adafika ku Nahaliyele, kuchokera ku Nahaliyele adafika ku Bamoti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kuchoka ku Matana anapita ku Nahalieli, kuchoka ku Nahalieli anapita ku Bamoti,

Onani mutuwo



Numeri 21:19
3 Mawu Ofanana  

chitsime adakumba mafumu, adachikonza omveka a anthu; atanena mlamuli, ndi ndodo zao. Ndipo atachoka kuchipululu anamuka ku Matana;


atachoka ku Bamoti ku chigwa chili m'dziko la Mowabu, ku mutu wa Pisiga, popenyana ndi chipululu.


Hesiboni ndi mizinda yake yonse yokhala pachidikha; Diboni, ndi Bamoti-Baala ndi Bete-Baala-Meoni;