Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 17:4 - Buku Lopatulika

Ndipo uziike m'chihema chokomanako, chakuno cha mboni, kumene ndikomana ndi inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo uziike m'chihema chokomanako, chakuno cha mboni, kumene ndikomana ndi inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ndodozo uziike m'chihema chamsonkhano patsogolo pa bokosi laumboni pamene ndimakumana nawe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Uyike ndodozo mu tenti ya msonkhano, kutsogolo kwa Bokosi la Umboni, kumene ndimakumana nawe.

Onani mutuwo



Numeri 17:4
7 Mawu Ofanana  

nupere china chisalale, nuchiike chakuno cha mboni m'chihema chokomanako, kumene ndidzakomana ndi iwe; uchiyese chopatulika ndithu.


Nuliike chakuno cha nsalu yotchinga ili ku likasa la mboni, patsogolo pa chotetezerapo chili pamwamba pa mboni, pomwe ndidzakomana ndi iwe.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Bweza ndodo ya Aroni kuiika chakuno cha mboni, isungike ikhale chizindikiro cha pa ana opikisana; kuti unditsirizire madandaulo ao, kuti ungafe.


Ndipo ulembe dzina la Aroni pa ndodo ya Levi; pakuti pakhale ndodo imodzi pa mkulu yense wa nyumba za makolo ao.


Ndipo Mose anaika ndodozo pamaso pa Yehova m'chihema cha mboni.