Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:8 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose ananena ndi Kora, Tamvani tsono, inu ana a Levi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose ananena ndi Kora, Tamvani tsono, inu ana a Levi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose adauza Kora kuti, “Imvani tsono inu Alevi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mose anawuzanso Kora kuti, “Inu Alevi, tsopano tamverani!

Onani mutuwo



Numeri 16:8
3 Mawu Ofanana  

nimuikemo moto, muikenso chofukiza pamenepo, pamaso pa Yehova, mawa; ndipo kudzali kuti amene Yehova amsankha, wopatulika ndiye; mwakula mphamvu, inu ana a Levi.


kodi muchiyesa chinthu chaching'ono, kuti Mulungu wa Israele anakusiyanitsani ku gulu la Israele, kukusendezani pafupi pa Iye, kuchita ntchito ya chihema cha Yehova, ndi kuima pamaso pa khamu kuwatumikira;


Ndipo Mika anamninkha zansembe Mleviyo, ndi mnyamatayo anakhala wansembe wake, nakhala m'nyumba ya Mika.