Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 16:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mose anawuzanso Kora kuti, “Inu Alevi, tsopano tamverani!

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 Ndipo Mose ananena ndi Kora, Tamvani tsono, inu ana a Levi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Mose ananena ndi Kora, Tamvani tsono, inu ana a Levi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mose adauza Kora kuti, “Imvani tsono inu Alevi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:8
3 Mawu Ofanana  

ndipo mawa muyikemo moto ndi lubani pamaso pa Yehova. Munthu amene Yehova amusankhe ndiye amene ali woyera. Alevi inu mwawonjeza kwambiri!”


Kodi sizinakukwanireni kuti Mulungu wa Israeli anakupatulani pakati pa gulu lonse la Aisraeli ndi kukubweretsani pafupi ndi Iye, kuti muzigwira ntchito ku nyumba ya Yehova ndi kumayima pamaso pa gulu, kumatumikira?


Pambuyo pake Mika anapatula Mleviyo ndipo mnyamatayu anakhala wansembe. Tsono ankakhala mʼnyumba ya Mika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa