Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yake ya zofukiza, naikamo moto, naikapo chofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wachilendo, umene sanawauze.
Numeri 16:6 - Buku Lopatulika Chitani ichi; dzitengereni mbale za zofukiza, Kora, ndi khamu lake lonse; Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Chitani ichi; dzitengereni mbale za zofukiza, Kora, ndi khamu lake lonse; Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Tsono iwe Kora, pamodzi ndi gulu lako lonse, muchite izi: mutenge zofukizira lubani, Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Iwe Kora pamodzi ndi onse amene akukutsatira chitani izi: Tengani zofukizira |
Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yake ya zofukiza, naikamo moto, naikapo chofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wachilendo, umene sanawauze.
nanena ndi Kora ndi khamu lake lonse, ndi kuti, M'mawa Yehova adzatizindikiritsa anthu ake ndi ayani, wopatulika ndani, amene adzamsendeza pafupi pa Iye; ndi iye amene anamsankha adzamsendeza pafupi pa Iye.
nimuikemo moto, muikenso chofukiza pamenepo, pamaso pa Yehova, mawa; ndipo kudzali kuti amene Yehova amsankha, wopatulika ndiye; mwakula mphamvu, inu ana a Levi.