Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:6 - Buku Lopatulika

Chitani ichi; dzitengereni mbale za zofukiza, Kora, ndi khamu lake lonse;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chitani ichi; dzitengereni mbale za zofukiza, Kora, ndi khamu lake lonse;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono iwe Kora, pamodzi ndi gulu lako lonse, muchite izi: mutenge zofukizira lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwe Kora pamodzi ndi onse amene akukutsatira chitani izi: Tengani zofukizira

Onani mutuwo



Numeri 16:6
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yake ya zofukiza, naikamo moto, naikapo chofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wachilendo, umene sanawauze.


nanena ndi Kora ndi khamu lake lonse, ndi kuti, M'mawa Yehova adzatizindikiritsa anthu ake ndi ayani, wopatulika ndani, amene adzamsendeza pafupi pa Iye; ndi iye amene anamsankha adzamsendeza pafupi pa Iye.


nimuikemo moto, muikenso chofukiza pamenepo, pamaso pa Yehova, mawa; ndipo kudzali kuti amene Yehova amsankha, wopatulika ndiye; mwakula mphamvu, inu ana a Levi.