Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 16:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iwe Kora pamodzi ndi onse amene akukutsatira chitani izi: Tengani zofukizira

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Chitani ichi; dzitengereni mbale za zofukiza, Kora, ndi khamu lake lonse;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Chitani ichi; dzitengereni mbale za zofukiza, Kora, ndi khamu lake lonse;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono iwe Kora, pamodzi ndi gulu lako lonse, muchite izi: mutenge zofukizira lubani,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:6
7 Mawu Ofanana  

Ana a Aaroni, Nadabu ndi Abihu, aliyense anatenga chofukizira lubani chake nayikamo makala a moto ndi kuthiramo lubani. Iwo anapereka pamaso pa Yehova moto wachilendo, moto umene Yehova sanawalamule.


Ndipo iye anawuza Kora ndi anthu onse amene ankamutsatira kuti, “Yehova mawa mmawa adzasonyeza yemwe ndi wake ndiponso amene ndi woyera mtima. Munthuyo adzabwera pafupi ndi Iye. Munthu amene adzamusankheyo adzamusendeza pafupi.


ndipo mawa muyikemo moto ndi lubani pamaso pa Yehova. Munthu amene Yehova amusankhe ndiye amene ali woyera. Alevi inu mwawonjeza kwambiri!”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa