Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:44 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo Chauta adauza Moseyo kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo



Numeri 16:44
4 Mawu Ofanana  

Arauna nati, Mbuye wanga mfumu, mwadzeranji kwa mnyamata wanu? Ndipo Davide, anati, Kugula dwale lako ili, kuti ndimangirepo Yehova guwa la nsembe, kuti mliriwo ulekeke kwa anthu.


Koma Iye pokhala ngwa chifundo, anakhululukira choipa, osawaononga; nabweza mkwiyo wake kawirikawiri, sanautse ukali wake wonse.


Ndipo Mose ndi Aroni anadza kukhomo kwa chihema chokomanako.


Kwerani kuchoka pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi. Pamenepo adagwa nkhope zao pansi.