Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:2 - Buku Lopatulika

Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mukakalowa m'dziko lokakhalamo inu, limene ndilikupatsa inu,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mukakalowa m'dziko lokakhalamo inu, limene ndilikupatsa inu,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Uza Aisraele kuti, ‘Mukadzaloŵa m'dziko limene ndidzakupatsenilo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukupatsanilo,

Onani mutuwo



Numeri 15:2
8 Mawu Ofanana  

Mutakafika m'dziko la Kanani, limene ndikupatsani likhale lanulanu, ndipo ndikaika nthenda yakhate m'nyumba ya dziko lanulanu;


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mutakalowa m'dziko limene ndikupatsani, ndi kucheka dzinthu zake, pamenepo muzidza nao mtolo wa zipatso zoyamba za masika anu kwa wansembe;


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mutakalowa m'dziko limene ndikupatsani, dzikoli lizisungira Yehova Sabata.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose nati,


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Pamene mulowa m'dziko limene ndilikukulowetsani,


Awa ndi malemba ndi maweruzo, muziwasamalirawa kuwachita m'dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani likhale lanulanu, masiku onse akukhala ndi moyo inu padziko lapansi.


pakuti mpaka lero simunafikire mpumulo ndi cholowa, zimene Yehova Mulungu wanu adzakupatsani.