Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:19 - Buku Lopatulika

kudzali, pakudya inu mkate wa m'dzikolo, muzikwezera Yehova nsembe yokweza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kudzali, pakudya inu mkate wa m'dzikolo, muzikwezera Yehova nsembe yokweza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo mukamadzadya buledi wam'dzikolo, mudzapereke nsembe kwa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo mukakadya chakudya cha mʼdzikolo, mukapereke gawo lina kwa Yehova monga chopereka.

Onani mutuwo



Numeri 15:19
3 Mawu Ofanana  

Ndipo wansembe mwana wa Aroni azikhala ndi Alevi, polandira Alevi limodzilimodzi la magawo khumi; ndi Alevi azikwera nalo limodzi la magawo khumi mwa limodzilimodzi la magawo khumi kunyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda, kunyumba ya chuma.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Pamene mulowa m'dziko limene ndilikukulowetsani,