Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:12 - Buku Lopatulika

Monga mwa kuwerenga kwake kwa izi muzikonza, muzitero ndi yonse monga mwa kuwerenga kwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Monga mwa kuwerenga kwake kwa izi muzikonza, muzitero ndi yonse monga mwa kuwerenga kwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zingachuluke chotani nyama zoperekedwazo, muchite choncho ndi nyama iliyonse, mpaka zonse kutha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngakhale zingachuluke chotani, chitani izi kwa iliyonse ya nyamazo.

Onani mutuwo



Numeri 15:12
2 Mawu Ofanana  

Kudzatero ndi ng'ombe iliyonse, kapena nkhosa yamphongo iliyonse, kapena mwanawankhosa aliyense, kapena mwanawambuzi aliyense.


Onse akubadwa m'dzikomo achite izi momwemo, pobwera nayo kwa Yehova nsembe yamoto ya fungo lokoma.