Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 13:11 - Buku Lopatulika

Wa fuko la Yosefe, wa fuko la Manase, Gadi mwana wa Susi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la Yosefe, wa fuko la Manase, Gadi mwana wa Susi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la Yosefe (ndiye kuti m'fuko la Manase) adatuma Gadi mwana wa Susi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera ku fuko la Manase (fuko la Yosefe), Gadi mwana wa Susi;

Onani mutuwo



Numeri 13:11
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anadalitsa iwo tsiku lomwelo, nati, Mwa iwe Israele adzadalitsa, kuti, Mulungu akuyese iwe monga Efuremu ndi monga Manase; ndipo anaika Efuremu woyamba wa Manase.


Wa fuko la Zebuloni, Gadiele mwana wa Sodi.


Wa fuko la Dani, Amiyele mwana wa Gemali.


Uma womwe ndi Afeki, ndi Rehobu; mizinda makumi awiri mphambu iwiri ndi midzi yao.