Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:9 - Buku Lopatulika

Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene mame ankagwa usiku pamahemapo, ankagwera kumodzi ndi mana.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mame akamagwa pa msasawo usiku ankagwera kumodzi ndi manawo.

Onani mutuwo



Numeri 11:9
6 Mawu Ofanana  

Anafunsa ndipo Iye anadzetsa zinziri, nawakhutitsa mkate wakumwamba.


Ndipo Mose anamva anthu alikulira m'mabanja ao, yense pakhomo pa hema wake; ndipo Yehova anapsa mtima ndithu, ndipo kudamuipira Mose.


Anthu amanka, nawaola, nawapera ndi mphero, kapena kuwasinja mumtondo, nawaphika m'mphika, nawaumba timitanda; ndi powalawa anali ngati timitanda tokazinga ndi mafuta.


Chiphunzitso changa chikhale ngati mvula; maneno anga agwe ngati mame; ngati mvula yowaza pamsipu, ndi monga madontho a mvula pazitsamba.