Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:30 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose ndi akulu onse a Israele anasonkhana kuchigono.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose ndi akulu onse a Israele anasonkhana kuchigono.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Mose ndi atsogoleri a Aisraele aja adabwerera ku mahema.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mose ndi akuluakulu a Israeli aja anabwerera ku msasa.

Onani mutuwo



Numeri 11:30
3 Mawu Ofanana  

Koma Mose anati kwa iye, Kodi uchita nsanje nao chifukwa cha ine? Mwenzi anthu onse a Yehova atakhala aneneri? Mwenzi Yehova atawaikira mzimu wake!


Ndipo kudachokera mphepo kwa Yehova, n'kudza nazo zinziri zochokera kunyanja, ndipo zidagwa kuchigono, ulendo wa tsiku limodzi dera lino, ndi ulendo wa tsiku limodzi dera lina, pozungulira pa chigono, ndipo zinabisa nthaka ngati muyeso wa mikono iwiri.


Ndipo Mose anauka namuka kwa Datani ndi Abiramu; ndi akulu a Israele anamtsata.