Popeza Yehova adalankhula ndi Mose, ndi kuti,
chifukwa Chauta adaauza Mose kuti,
Pakuti Yehova anawuza Mose kuti,
Koma Alevi monga mwa fuko la makolo ao sanawerengedwe mwa iwo.
Fuko la Levi lokha usaliwerenge, kapena kuona kufikira kwao mwa ana a Israele;