Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:10 - Buku Lopatulika

Ana a Ara, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana a Ara, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

A banja la Ara 652.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zidzukulu za Ara 652

Onani mutuwo



Nehemiya 7:10
4 Mawu Ofanana  

Ana a Ara, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi awiri kudza asanu.


Pakuti ambiri mu Yuda analumbirirana naye chibwenzi; popeza ndiye mkamwini wake wa Sekaniya mwana wa Ara; ndi mwana wake Yehohanani adadzitengera mwana wamkazi wa Mesulamu mwana wa Berekiya.


Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi limodzi ndi asanu ndi atatu.


Ana a Sefatiya, mazana atatu mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.