Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 2:5 - Buku Lopatulika

5 Ana a Ara, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi awiri kudza asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ana a Ara, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi awiri kudza asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 A banja la Ara, 775.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 zidzukulu za Ara 775

Onani mutuwo Koperani




Ezara 2:5
3 Mawu Ofanana  

Ana a Sefatiya, mazana atatu mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.


Pakuti ambiri mu Yuda analumbirirana naye chibwenzi; popeza ndiye mkamwini wake wa Sekaniya mwana wa Ara; ndi mwana wake Yehohanani adadzitengera mwana wamkazi wa Mesulamu mwana wa Berekiya.


Ana a Ara, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa