Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 7:9 - Buku Lopatulika

Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndani mwa inu, mwana wake atampempha buledi, iye nkumupatsa mwala?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ndani mwa inu, mwana wake akamupempha buledi amamupatsa mwala?

Onani mutuwo



Mateyu 7:9
3 Mawu Ofanana  

Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?


pakuti yense wakupempha alandira; ndi wakufunayo apeza; ndi kwa wogogodayo chitsegulidwa.