Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:2 - Buku Lopatulika

Ufumu wa Kumwamba ufanafana ndi munthu, mfumu, amene anakonzera mwana wake phwando la ukwati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ufumu wa Kumwamba ufanafana ndi munthu, mfumu, amene anakonzera mwana wake phwando la ukwati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Za Ufumu wakumwamba tingazifanizire motere: Mfumu ina idaakonzera mwana wake phwando laukwati.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ufumu wakumwamba uli ngati mfumu imene inakonzera phwando mwana wake wamwamuna.

Onani mutuwo



Mateyu 22:2
15 Mawu Ofanana  

Fanizo lina Iye anawafotokozera iwo, nanena, Ufumu wa Kumwamba ufanizidwa ndi munthu, amene anafesa mbeu zabwino m'munda mwake;


Ndipo Yesu anayankha, nalankhulanso kwa iwo m'mafanizo, nati,


ndipo inu nokha khalani ofanana ndi anthu oyembekezera mbuye wao, pamene ati abwera kuchokera kuukwati; kuti pakudza iye, nakagogoda, akamtsegulire pomwepo.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Pakuti ndichita nsanje pa inu ndi nsanje ya Mulungu; pakuti ndinakupalitsani ubwenzi mwamuna mmodzi, kuti ndikalangize inu ngati namwali woyera mtima kwa Khristu.


Ndipo muchite monga momwe ananena mau akufotokozeraniwo, ku malo amene Yehova adzawasankha; nimusamalire kuchita monga mwa zonse akulangizanizi.