Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 20:9 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene iwo olembedwa poyandikira madzulo anadza, analandira munthu aliyense rupiya latheka limodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene iwo olembedwa poyandikira madzulo anadza, analandira munthu aliyense rupiya latheka limodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene adabwera olembedwa pa 5 koloko yamadzulo aja, aliyense adalandira ndalama imodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Antchito amene anawalemba ganyu pa 5 koloko masana anafika ndipo aliyense analandira dinari.

Onani mutuwo



Mateyu 20:9
10 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene oyamba anadza, analingalira kuti adzalandira kopambana, ndipo iwonso analandira onse rupiya latheka.


Ndipo pamene adapangana ndi antchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza kumunda wake.


Ndipo pamadzulo, mwini munda anati kwa kapitao wake, Kaitane antchito, nuwapatse iwo kulipira kwao, uyambe kwa omalizira kufikira kwa oyamba.