Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 19:2 - Buku Lopatulika

Ndipo makamu aakulu a anthu anamtsata; ndipo Iye anawachiritsa kumeneko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo makamu akulu a anthu anamtsata; ndipo Iye anawachiritsa kumeneko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu ambirimbiri adamtsata, ndipo Iye ankachiritsa odwala kumeneko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Magulu akulu a anthu anamutsatira Iye, ndipo iwo anachiritsidwa pomwepo.

Onani mutuwo



Mateyu 19:2
7 Mawu Ofanana  

Koma Yesu m'mene anadziwa, anachokera kumeneko: ndipo anamtsata Iye anthu ambiri; ndipo Iye anawachiritsa iwo onse,


Ndipo Afarisi anadza kwa Iye, namuyesa, nanena, Kodi nkuloledwa kuti munthu achotse mkazi wake pa chifukwa chilichonse?